Mawu a M'munsi
a M’Baibulo, mawu akuti “malangizo” amatanthauza kuphunzitsa, kutsogolera komanso kuthandiza munthu kuti asinthe. Koma satanthauza kuzunza kapena kuchitira munthu nkhanza.—Miyambo 4:1.
a M’Baibulo, mawu akuti “malangizo” amatanthauza kuphunzitsa, kutsogolera komanso kuthandiza munthu kuti asinthe. Koma satanthauza kuzunza kapena kuchitira munthu nkhanza.—Miyambo 4:1.