Mawu a M'munsi
a Chifupifupi zaka 150 pambuyo pa masomphenya a Ezekieli, wolemba mbiri wa Chigriki Herodotus, pozindikira kuti zizindikiro pa anthu odzipereka kwa mulungu Hercules zinapereka kwa iwo chlnjirizo, analemba: “Ngati kapolo wa munthu wina aliyense apeza chinjirizo [mu kachisi wa Hercules], ndipo chizinddoro chopatulika chiikidwa pa iye, chotero kudzipereka iye mwini kwa mulungu, sichiri chalamulo kupha munthu ameneyo.