Mawu a M'munsi
a Malinga ndi kunena kwa Talmud, arabi akale analangiza kuti: “Wophunzira sayenera kulankhula ndi mkazi mkhwalala.” Ngati mwambo umenewu unalipo mtsiku la Yesu, mwinamwake chingakhale chifukwa chimene ophunzira ake “anazizwa kuti anali kulankhula ndi mkazi.”—Yohane 4:27.