Mawu a M'munsi
c Otembenuza ambiri amakono amalephera kuzindikira liwu lobwerezedwabwerezedwa la Chihebri pano lokhala ndi tanthauzo lofanana. Chotero m’malo mwa “dzuzunda . . . dzuzunda” (New World Translation; Revised Standard Version), iwo amagwiritsira ntchito “kuphwanya . . . kukantha” (The Jerusalem Bible; New International Version), “kuphwanya . . . kuluma” (Today’s English Version), “kuponda. . . kukantha” (Lamsa), kapena “kuphwanya . . . kulalira” (Knox).