Mawu a M'munsi
a Mu Palestina, mphesa zinali kututidwa kumapetokwa chirimwe. Komabe, Paskha wa Chiyuda ndiMgonero wa Ambuye, zinali kuchitika mu ngululu—miyezi isanu ndi umodzi pambuyo pake. Popanda njira ya kusungira, madzi a mphesa mwachibadwa angawole.