Mawu a M'munsi
a Dr. E. H. Plumptre akulongosola kuti: “[Kugwiritsira ntchito mu King James Version] kumasonyeza lingaliro la kukambitsirana pakati pa anthu ofanana. Chihebri chimasonyeza kutuluka kwa mawu kwa amene akupanga ulamuliro wapamwamba, monga ngati kuchokera kwa woweruza akulankhula kwa wozengedwa mlandu.”