Mawu a M'munsi
a Liwu la Chihebri kaamba ka zosema zochitidwa manyazi gil·lu·limʹ, linali liwu lonyodola limene poyambirira linatanthauza “mibulu ya tudzi”—chinachake chonyansa kwa Ayuda.—Deuteronomo 23:12-14; 1 Mafumu 14:10; Ezekieli 4:12-17.
a Liwu la Chihebri kaamba ka zosema zochitidwa manyazi gil·lu·limʹ, linali liwu lonyodola limene poyambirira linatanthauza “mibulu ya tudzi”—chinachake chonyansa kwa Ayuda.—Deuteronomo 23:12-14; 1 Mafumu 14:10; Ezekieli 4:12-17.