Mawu a M'munsi
a Verebu la Chigriki kaamba ka “kubweretsa mbiri yabwino,” kapena “kulengeza,” (eu·ag·ge·liʹzo·mai) limabwera kuchokera kukaimidwe ka liwu la Chihebri lotchulidwa ‘kubweretsa mbiri yabwino’ (bis·sarʹ) mu Yesaya 52:7. Verebu lakuti bis·sarʹ pano limatanthauza “kubukitsa chipambano cha chilengedwe chonse cha Yahweh padziko lapansi ndi ulamuliro wake wa ufumu” ndi kubadwa kwa mbadwo watsopano, imanena tero The New International Dictionary of New Testament Theology.—Yerekezani ndi Nahumu 1:15, New World Translation of the Holy Scriptures—With References, mawu a m’munsi.