Mawu a M'munsi
c Iyi inali imodzi ya nkhondo zosankha zomenyedwa pa Megido, yomwe inatsogolera ku kukhala kwake chizindikiro cha nkhondo yosankha yomalizira ya Mulungu motsutsana ndi mitundu ya anthu yowukira pa Harmagedo, kapena pa Armagedo.—Chivumbulutso 16:16.