Mawu a M'munsi
a Ponena za masiku, timavomereza ndandanda ya masiku yomwe imapezeka m’Baibulo, imene panthaŵi zina imasiyana ndi masiku amakedzana ozikidwa pa magwero osadalirika kwenikweni a ku dziko. Kaamba ka kukambitsirana kwatsatanetsatane kwa ndandanda ya masiku ya Baibulo, onani bukhu la Aid to Bible Understanding, masamba 322-48.