Mawu a M'munsi
b “Lingaliro la pangano linali mbali yapadera ya chipembedzo cha Israyeli, yokhayo yofuna kukhulupirika kotheratu ndi kuthetsa kuthekera kwa kukhulupirika kuŵiri kapena kochulukira konga komwe kunaloledwa m’zipembedzo zina.”—Theological Dictionary of the Old Testament, Volyumu II, tsamba 278.