Mawu a M'munsi
a “Ngakhale masinthidwe opambana koposa anasiya nzika zosauka, okhala ndi mwaŵi mopambanitsa, otchuka olipiritsidwa msonkho wochepera, gulu lapakati linalowerera mosakwanira m’boma ndiponso m’chitaganya . . . Chiyenera kunenedwa kuti pamene kuli kwakuti malo a unduna owunikiridwa anayamba kuyang’anizana ndi mafunso omwe sakanakhoza kunyalanyazidwanso, iwo sakanakhoza kupereka chothetsera chenicheni mkati mwa zenizeni za ndale zadziko ndi chuma cha nyengoyo.”—Western Civilization—Its Genesis and Destiny: The Modern Heritage.