Mawu a M'munsi
b Yesu sali mbali ya pangano latsopano. Iye ali Nkhoswe yake ndipo alibe machimo ofunikira kukhululukidwa. Kuwonjezerapo, sichiri choyenerera kaamba ka iye kukhala mfumu-wansembe ndi ilo, popeza kuti iye ali mfumu mogwirizana ndi pangano la Davide ndiponso wansembe mofanana ndi Melikizedeke.