Mawu a M'munsi
a Ngakhale lerolino sikukuvomerezedwa kumvetsera ndi kuwanditsa mphekesera wamba (zimene kaŵirikaŵiri ziribe maumboni alionse) ponena za zimene ziŵalo za Bungwe Lolamulira kapena oimira awo ayerekezeredwa kukhala atanena kapena kuchita.