Mawu a M'munsi
b “Mu mkhalidwe wofutukulidwa lamulo lake lingalongosoledwe kukhala: ‘Musapange unansi uliwonse, kaya wakanthaŵi kapena wokhalitsa, ndi osakhulupirira womwe ungatsogolere ku kulolera molakwa miyezo Yachikristu kapena kufooketsa kukhazikika kwa mboni Yachikristu. Ndipo nchifukwa ninji kulekana koteroko? Chifukwa chakuti wosakhulupirira alibe phande m’miyezo, zisoni, kapena zonulirapo za Mkristuyo.’”—The Expositor’s Bible Commentary, Volyumu 10, tsamba 359.