Mawu a M'munsi
a Mosangalatsa, pa Miyambo 2:5 mawu akuti “chidziŵitso chenicheni cha Mulungu” amapezeka mu Septuagint Yachigriki kukhala e·piʹgno·sis, kapena “chidziŵitso cholongosoka,” kumodzi kwa kugwiritsira ntchito kusanu ndi kutatu kwa liwu Lachigriki limenelo mu Septuagint.