Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Ophunzira Baibulo ambiri amazindikira kuti nthanthi imeneyi njolakwa, popeza kuti Malemba Achigriki, olembedwa m’zaka za zana loyamba C.E., amalemba kukwaniritsidwa kwa maulosi ambiri a Malemba Achihebri, amene mowonekera analembedwa zaka mazana ambiri kalelo. Mwachitsanzo, kukwaniritsidwa kwa m’zaka za zana loyamba kwa tsatanetsatane wa Danieli 9:24-27 kwalembedwa kaya m’Malemba Achigriki kapena ndi akatswiri a mbiri yakale yakudziko.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena