Mawu a M'munsi
a “Pausiku umene Iye anaperekedwa Ambuye Yesu anatenga mkate; atayamika, anaunyema nati: ‘Iri ndithupi langa kaamba ka inu; chitani ichi monga chondikumbukira.’ Mofananamo Iye anatenga chikho pamene chakudya chamadzulo chinali chitatha, ndipo adaati: ‘Chikho ichi ndicho pangano latsopano, lotsimikiziridwa ndi mwazi wanga; nthaŵi iriyonse imene muchimwa, mutero kundikumbukira.’”—An Expanded Paraphrase of the Epistles of Paul, lolembedwa ndi F. F. Bruce.