Mawu a M'munsi
b Katswiri wina akupereka lingaliro iri ponena za chifukwa chimene vinyo anawonjezeredwera: “[Paskha] siidafunikirenso kukhala mwambo wachaka ndi chaka wa kusonkhana kwa amuna achikulire; iyo inafunikira kukhala chochitika cha phwando labanja, m’limene kumwa vinyo kunali kwachibadwa.”—The Hebrew Passover—From the Earliest Times to A.D. 70, lolembedwa ndi J. B. Segal.