Mawu a M'munsi
a Kukhala woleza mtima sikumatanthauza kungovutika kwa nthaŵi yaitali. Ngati munthu wovutika kwa nthaŵi yaitali anakwiyitsidwa kapena kuipidwa chifukwa chakuti sakhoza kubwezera, iye sangakhale woleza mtima.
a Kukhala woleza mtima sikumatanthauza kungovutika kwa nthaŵi yaitali. Ngati munthu wovutika kwa nthaŵi yaitali anakwiyitsidwa kapena kuipidwa chifukwa chakuti sakhoza kubwezera, iye sangakhale woleza mtima.