Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b Osati kale kwambiri ofalitsa nkhani ku United States anabukitsa zochititsa manyazi za mlaliki wa pa TV, pamene mkazi wake yemwe ndi ngwazi inzake anakoka pafupifupi chisamaliro chachikulu. Mogwirizana ndi malipoti a nyuzi, iye anakula akukhulupirira kuti “zonse ziŵiri zodzoladzola ndi akanema” nzoipa, komabe pambuyo pake anasintha lingaliro lake ndipo anadzadziŵika chifukwa chogwiritsira ntchito “zodzoladzola zochulukitsitsa zomwe zinawoneka ngati zosema.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena