Mawu a M'munsi
b Osati kale kwambiri ofalitsa nkhani ku United States anabukitsa zochititsa manyazi za mlaliki wa pa TV, pamene mkazi wake yemwe ndi ngwazi inzake anakoka pafupifupi chisamaliro chachikulu. Mogwirizana ndi malipoti a nyuzi, iye anakula akukhulupirira kuti “zonse ziŵiri zodzoladzola ndi akanema” nzoipa, komabe pambuyo pake anasintha lingaliro lake ndipo anadzadziŵika chifukwa chogwiritsira ntchito “zodzoladzola zochulukitsitsa zomwe zinawoneka ngati zosema.”