Mawu a M'munsi
a Nthaŵi imene Roy Ryan anali kulemba zokumana nazo za moyo wake, umoyo wake unaipirako. Iye anamaliza ntchito yake yapadziko lapansi pa July 5, 1991, pasanapite nthaŵi yaitali pambuyo pakuchita mbali yake monga wotsogoza wa kulambira kwa m’maŵa pa Watchtower Farms.