Mawu a M'munsi
a Profesa Paul Haupt anafotokoza kuti: ‘M’nthanthi za m’zaka za mazana apakati nyanga za chipembere kapena minyanga ya narwhal (yotchedwanso nsomba yanyanga imodzi kapena namgumi wanyanga imodzi) zinkalingaliridwa kukhala nyanga za kavalo wanyanga imodzi.’