Mawu a M'munsi
b Monga momwe kunasonyezedwera m’nkhani zapitazo za mpambo uno, ngakhale kuti Theophilus ndi Tertullian anagwiritsira ntchito mawu amenewo, iwo sanalingalire za Utatu umene umakhulupiriridwa ndi Chikristu Chadziko lerolino.
b Monga momwe kunasonyezedwera m’nkhani zapitazo za mpambo uno, ngakhale kuti Theophilus ndi Tertullian anagwiritsira ntchito mawu amenewo, iwo sanalingalire za Utatu umene umakhulupiriridwa ndi Chikristu Chadziko lerolino.