Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a “‘Dama’ m’lingaliro lotakata, ndipo monga lagwiritsiridwa ntchito pa Mateyu 5:32 ndi 19:9, mwachiwonekere limasonya ku mitundu yambiri yamaunansi akugonana kosaloledwa ndi lamulo kapena koswa lamulo kwakunja kwaukwati. Porneia [liwu Lachigiriki logwiritsidwa ntchito m’malemba amenewo] limaphatikizapo kugwiritsidwa ntchito koipa kwa mpheto kochitidwa ndi munthu mmodzi kapena oposerapo (kaya kukhale mwanjira yachibadwa kapena yoluluzika); ndiponso, payenera kukhala panali chiŵalo china m’chisembwerecho​—mwamuna kapena mkazi, kapena nyama.” (Nsanja ya Olonda, September 1, 1983, tsamba 31) Chigololo ndicho: “Kugonana kodzifunira pakati pa munthu wokwatira ndi munthu wina wosakhala mwamuna kapena mkazi wake walamulo.”​—The American Heritage Dictionary of the English Language.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena