Mawu a M'munsi
a M’Chigiriki, liwu lakuti “chokhumudwitsa” (σκάνδαλον, skanʹda·lon) poyambirira “linali dzina la mbali ya msampha kumene nyambo inaikidwako, chotero, linatchula msampha weniweniwo kapena diŵa.”—Vine’s Expository Dictionary of Old and New Testament Words.