Mawu a M'munsi
a Upandu wina umene ma bulletin board amenewo ali nawo ndiwo chiyeso cha kuika m’kompyuta yanu maprogramu ndi mabuku amene eni ake kapena owalemba samawalola kulembedwanso, kumene kungakhale kusemphana ndi malamulo a padziko lonse oletsa kulembanso zimene ena analemba.—Aroma 13:1.