Mawu a M'munsi
a Webster’s Ninth New Collegiate Dictionary imamasulira “njirisi” kukhala “chithumwa (monga chokometsera) chimene kaŵirikaŵiri chimalembedwa ndi mawu amatsenga kapena chizindikiro kuti chichinjirize wochivalayo ku zoipa (monga ngati matenda kapena ufiti) kapena kumthandiza.”