Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Kuvutika kwakukulu kumene Yesu anapirira mwinamwake kungaonedwe m’chenicheni chakuti munthu wangwiroyo anamwalira pambuyo pa maola oŵerengeka chabe pamtengo wozunzirapo, pamene kuli kwakuti ochita zoipa amene anapachikidwa pamodzi naye anafunikira kuthyoledwa miyendo yawo kufulumizitsa imfa yawo. (Yohane 19:31-33) Iwo sanamve kuvutika kwa maganizo ndi kwakuthupi kofanana ndi kumene Yesu anali nako mkati mwa zochitika za kuimbidwa mlandu usiku wonse asanapachikidwe, mwinamwake kufikira pamlingo wakuti sakanathanso kunyamula mtengo wake wozunzirapo.​—Marko 15:15, 21.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena