Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b Novatian akusonyeza mfundo yakuti liwu lotanthauza “amodzi” m’vesili silimasonyeza kuti ali amodzi muumuna kapena ukazi. Chotero, tanthauzo lake lachibadwa nlakuti ali “chinthu chimodzi.” Yerekezerani ndi Yohane 17:21, pamene liwu Lachigiriki lotembenuzidwa “amodzi” lagwiritsiridwa ntchito m’njira imodzimodziyo. Mokondweretsa, New Catholic Encyclopedia (kope la mu 1967) kwakukulukulu imavomereza De Trinitate ya Novatian, ngakhale kuti imanena kuti “Mzimu Woyera sukulingaliridwa kukhala Munthu waumulungu.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena