Mawu a M'munsi
b Magazini a World Press Review a November 1992 anali ndi nkhani yochokera mu The Toronto Star imene inati: “M’zaka zingapo zapitazo, nzika za ku Russia zapenyereradi kuwonongeka kwa malingaliro onyenga amphamvu a mbiri ya dziko lawo. Koma kutulukiridwa kwa mgwirizano wa tchalitchi ndi boma la chikomyunizimu kwapereka nkhonya yowononga koposa.”