Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

d Mawu akuti “mpaka nthaŵi ya mapeto” angatanthauze “m’nthaŵi ya chitsiriziro.” Liwu lotembenuzidwa pano kuti “mpaka” limaonekera m’malembo Achiaramu pa Danieli 7:25 ndipo pamenepo limatanthauza kuti “m’nthaŵi” kapena “kwa.” Liwulo lili ndi tanthauzo lofananalo m’malembo Achihebri pa 2 Mafumu 9:22, Yobu 20:5, ndi Oweruza 3:26. Komabe, m’matembenuzidwe ochuluka a Danieli 11:35, limamasuliridwa kuti “mpaka,” ndipo ngati liwuli lili lolondola, pamenepo “nthaŵi ya mapeto” yotchulidwa pano iyenera kukhala nthaŵi ya mapeto a chipiriro cha anthu a Mulungu.​—Yerekezerani ndi “Your Will Be Done on Earth,” patsamba 286.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena