Mawu a M'munsi
b Mwanjira ina, mbiri ‘yochokera kumpoto’ ingakhale ikuchokera kwa Yehova, polingalira za mawu ake kwa Gogi: “Ndidzakutembenuza . . . kukowa m’chibwano mwako ndi zokowera ndi kukutulutsa.” “Ndidzakutembenuza, . . . kukweza iwe uchoke kumalekezero a kumpoto; ndipo ndidzadza nawe kumapiri a Israyeli.”—Ezekieli 38:4; 39:2; yerekezerani ndi Salmo 48:2.