Mawu a M'munsi
b Kuti mupeze kukambitsiridwa kwatsatanetsatane kwa chifukwa chimene Mulungu walolera kuipa, onani buku lakuti Mungathe Kukhala ndi Moyo Kosatha m’Paradaiso pa Dziko Lapansi, lofalitsidwa ndi Watchtower Bible and Tract Society of New York, Inc.