Mawu a M'munsi
a Chimodzi cha zofalitsidwa zimenezo ndicho buku lakuti Mankind’s Search for God, lofalitsidwa mu 1990 ndi Watchtower Bible and Tract Society of New York, Inc. Anthu ambiri ayamikira mafotokozedwe ake anzeru ndi aukatswiri a zipembedzo zazikulu za m’dziko.