Mawu a M'munsi
a Kaŵirikaŵiri Baibulo limagwiritsira ntchito mneni Wachihebri wakuti cha·taʼʹ ndi mneni Wachigiriki wakuti ha·mar·taʹno kutanthauza “uchimo.” Mawu aŵiri ameneŵa amatanthauza “kuphonya,” m’lingaliro la kuphonya kapena kusafika pa chonulirapo, chizindikiro, kapena chandamale.