Mawu a M'munsi
a Chidziŵitso chachifupi chosonyeza ndalama zopereka zaufulu zimene zinalandiridwa ndiponso zinthu zimene zinagulidwa chimaŵerengedwa pamisonkhano yaikulu ndiponso kamodzi pamwezi m’mipingo. Panthaŵi ndi nthaŵi makalata odziŵitsa za mmene zoperekazo zikugwiritsidwira ntchito amatumizidwa. Motero aliyense amakumbutsidwa za mkhalidwe wa ndalama za ntchito yapadziko lonse ya Mboni za Yehova.