Mawu a M'munsi
b A deist ananena kuti, mofanana ndi wopanga watchi, Mulungu anayambitsa chilengedwe chake nachisiya choncho, osakhala ndi chochita nacho. Malinga ndi kunena kwa buku lakuti The Modern Heritage, a deist “anakhulupirira kuti kukana Mulungu kunali cholakwa chochititsidwa ndi kuthedwa nzeru, ndi kuti koma ulamuliro wopondereza wa Tchalitchi cha Katolika ndi kuumitsa zinthu ndi kusalolera kwa ziphunzitso zake ndiko kunali koipitsitsa.”