Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b A deist ananena kuti, mofanana ndi wopanga watchi, Mulungu anayambitsa chilengedwe chake nachisiya choncho, osakhala ndi chochita nacho. Malinga ndi kunena kwa buku lakuti The Modern Heritage, a deist “anakhulupirira kuti kukana Mulungu kunali cholakwa chochititsidwa ndi kuthedwa nzeru, ndi kuti koma ulamuliro wopondereza wa Tchalitchi cha Katolika ndi kuumitsa zinthu ndi kusalolera kwa ziphunzitso zake ndiko kunali koipitsitsa.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena