Mawu a M'munsi
a Ena angapemphere kwa Yesu chifukwa amakhulupirira kuti iye ndi Mulungu. Koma Yesu anali Mwana wa Mulungu, ndipo iyemwini analambira Yehova, Atate wake. (Yohane 20:17) Kuti mupeze malongosoledwe atsatanetsatane a nkhaniyi, onani Kodi Muyenera Kukhulupirira Utatu?, yofalitsidwa ndi Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania.