Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Pamene Yesu amalankhula za Ufumu wokonzedwa “pa chikhazikiro chake cha dziko lapansi” (Mateyu 25:34), ayenera kukhala akusonya nthaŵi ina ya pambuyo pa tchimo loyambalo. Luka 11:50, 51 amagwirizanitsa “kukhazikika kwa dziko lapansi,” kapena kukhazikitsidwa kwa mtundu wa anthu wowomboleka ndi dipo, ndi nthaŵi ya Abele.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena