Mawu a M'munsi
e Maimonides analongosola malamulo ameneŵa m’buku lake la Commentary on the Mishnah, (Sanhedrin 10:1). Pambuyo pake Chiyuda chinawalandira monga mpambo wololedwa wa zikhulupiriro. Mawu ali pamwambapo ndi chidule cha amene ali m’buku la mapemphero Lachiyuda.