Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Kwenikweni, iwo ananyoza osauka ndi mawu achipongwe akuti “ʽam-ha·ʼaʹrets,” kapena “anthu apansi.” Malinga ndi katsŵiri wina, Afarisi anaphunzitsa kuti munthu sayenera kuikizira chuma kwa anthu ameneŵa, kapena kukhulupirira umboni wawo, kapena kuwachereza monga alendo, kapena kukhala alendo awo, kapenanso kugula zinthu kwa iwo. Atsogoleri achipembedzo ananena kuti kukwatiwa kwa mwana wamkazi wa munthu kwa anthu ameneŵa kukakhala ngati kumpereka ku chilombo ali wonjatidwa ndi wopanda thandizo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena