Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a M’Malemba Achihebri monse, amuna ndi akazi a mu ukwati kaŵirikaŵiri amatchedwa monga “mwamuna” (Chihebri, ʼish) ndi “mkazi” (Chihebri, ʼish·shahʹ). Mwachitsanzo, mu Edene, mawu amene Yehova anagwiritsira ntchito anali, osati “mwini” ndi ‘wa mwini,’ koma “mwamuna” ndi “mkazi.” (Genesis 2:24; 3:16, 17) Ulosi wa Hoseya unaneneratu kuti atabwerako ku ukapolo, Israyeli molapa akatcha Yehova kuti “Mwamuna wanga,” ndipo osatinso ‘mwini wake wa ine.’ Zimene zikupereka lingaliro lakuti liwulo “mwamuna” linali lopereka lingaliro lachikondi kwambiri kuposa lakuti “mwini.”​—Hoseya 2:16.

Mabuku a Chichewa (1974-2026)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena