Mawu a M'munsi
b Buku lakuti Palestine in the Time of Christ likunena kuti: “M’zochitika zina, mkazi anali kuonedwa ngati kapolo. Mwachitsanzo, iye analetsedwa kupereka umboni m’bwalo lachiweruzo, kusiyapo kupereka umboni wa imfa ya mwamuna wake.” Ponena za Levitiko 5:1, The Mishnah ikufotokoza kuti: “[Lamulo lonena za] ‘lumbiro la umboni’ limagwira ntchito kwa amuna koma osati kwa akazi.”—Shebuoth 4:I.