Mawu a M'munsi
c Wolemba mbiri Wachiyuda wa m’zaka za zana loyamba Josephus akusimba kuti mlongo wake wa Mfumu Herode, Salome anatumizira mwamuna wake “chikalata chothetsa ukwati wawo, chinthu chimene chinali chosagwirizana ndi lamulo Lachiyuda. Pakuti kwa ife mwamuna (yekha) ndiye amene amaloledwa kuchita zimenezi.”—Jewish Antiquities, XV, 259 [vii, 10].