Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Onani kuti zimenezi zisanachitike, Yakobo anali atachitapo kanthu kale mwamphamvu kutetezera banja lake pa chisonkhezero cha Akanani. Anamanga guwa la nsembe, limene mosakayikira linamsiyanitsa ndi anansi ake Achikanani. (Genesis 33:20; Eksodo 20:24, 25) Ndiponso, anaimika hema wake kunja kwa mzinda wa Sekemu ndi kukumba chitsime cha iye mwini. (Genesis 33:18; Yohane 4:6, 12) Motero Dina ayenera kukhala atadziŵa bwino za chikhumbo cha Yakobo chakuti asayanjane ndi Akanani.

Mabuku a Chichewa (1974-2026)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena