Mawu a M'munsi
d “Makamu a anthu” osakhulupirikawo sindiwo a ʽam-ha·ʼaʹrets, kapena “anthu apansi,” amene atsogoleri achipembedzo odzikuza anakana kuyanjana nawo, koma amene Yesu ‘anagwidwa nawo mtima ndi chisoni.’—Mateyu 9:36; Yohane 7:49.
d “Makamu a anthu” osakhulupirikawo sindiwo a ʽam-ha·ʼaʹrets, kapena “anthu apansi,” amene atsogoleri achipembedzo odzikuza anakana kuyanjana nawo, koma amene Yesu ‘anagwidwa nawo mtima ndi chisoni.’—Mateyu 9:36; Yohane 7:49.