Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Mwa kufufuza kwake deralo, katswiri wa zaulimi Walter C. Lowdermilk (woimira Food and Agriculture Organization ya United Nations) anati: “Dzikoli kale linali paradaiso wa zifuyo.” Ndiponso ananena kuti mkhalidwe wake wakunja sunasinthe kwenikweni “chiyambire nthaŵi za Aroma,” ndipo “‘chipululu’ chimene chinakuta dziko limene linali lachonde chinakhalako chifukwa cha munthu, osati chilengedwe.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena