Mawu a M'munsi
c Liwu lachihebri la “mzimu,” ruʹach, limatanthauza “mpweya” kapena “mphepo.” Ponena za anthu, silimatanthauza chinthu choganiza chauzimu, koma m’malo mwake, malinga ndi kunena kwa The New International Dictionary of New Testament Theology, limatanthauza “mphamvu ya moyo ya munthu.”