Mawu a M'munsi
d Iye sanali womalizira kulingalira m’njira yachilendo imeneyo. Kuchiyambi kwa zaka za zana lino, wasayansi wina ananena kuti anapima kulemera kwa sou za anthu angapo mwa kuchotsa kulemera kwawo atangomwalira pa kulemera kwawo atakhala pafupi kumwalira.